Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 10:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo mbale wa atate wa Saulo anati, Undiuze chimene Samuele analankhula nawe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo mbale wa atate wa Saulo anati, Undiuze chimene Samuele analankhula nawe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Apo mbale wa bambo wakeyo adati, “Ndikukupempha, uzeko zimene adanena Samuele.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Amalume ake a Sauli anati, “Chonde, ndifotokozereniko zimene Samueli wakuwuzani.”

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 10:15
3 Mawu Ofanana  

Ndipo akulu onse anadza kwa Yeremiya, namfunsa; ndipo iye ananena nao monga mwa mau onsewo anamuuza mfumu. Ndipo analeka kunena naye; pakuti sikunamveke mlandu.


Ndipo mbale wa atate wake wa Saulo ananena kwa iye ndi mnyamata wake, Munanka kuti? Ndipo iye anati, Kukafuna abuluwo; ndipo pakuona kuti sitinawapeze, tinadza kwa Samuele.


Ndipo Saulo anati kwa mbale wa atate wake, Anatiuza momveka kuti abuluwo anapezedwa kale. Koma sanamdziwitse mau aja Samuele ananena za ufumuwo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa