Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 1:27 - Buku Lopatulika

27 Ndinampempha mwanayu; ndipo Yehova anandipatsa chopempha changa ndinachipempha kwa Iye;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Ndinampempha mwanayu; ndipo Yehova anandipatsa chopempha changa ndinachipempha kwa Iye;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Mwana uyu ndidachita kupempha, ndipo Chauta wandipatsa chopempha changacho.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Ndinapempha mwana uyu, ndipo Yehova wandipatsa chimene ndinamupempha.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 1:27
11 Mawu Ofanana  

Ndipo Yabezi anaitana kwa Mulungu wa Israele, ndi kuti, Mundidalitse ndithu, ndi kukulitsa malire anga; ndi dzanja lanu likhale ndi ine, nimundisunge, kuti choipa chisandivute. Ndipo Mulungu anafikitsa chopempha iye.


M'mene ndinasautsika ndinaitanira pa Yehova; anandiyankha nandiika motakasuka Yehova.


Ndinafuulira kwa Yehova mu msauko wanga, ndipo anandivomereza.


Wamva Yehova kupemba kwanga; Yehova adzalandira pemphero langa.


Masiku onse a kusala kwake akhala wopatulikira kwa Yehova.


Pemphani, ndipo chidzapatsidwa kwa inu; funani, ndipo mudzapeza; gogodani, ndipo chidzatsegulidwa kwa inu;


ndipo ngati tidziwa kuti atimvera chilichonse tichipempha, tidziwa kuti tili nazo izi tazipempha kwa Iye.


Ndipo Eli anadalitsa Elikana ndi mkazi wake, nati, Yehova akupatse mbeu ndi mkazi uyu m'malo mwa iye amene munampempha kwa Yehova. Ndipo iwowa anabwera kwao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa