1 Samueli 1:27 - Buku Lopatulika27 Ndinampempha mwanayu; ndipo Yehova anandipatsa chopempha changa ndinachipempha kwa Iye; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndinampempha mwanayu; ndipo Yehova anandipatsa chopempha changa ndinachipempha kwa Iye; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Mwana uyu ndidachita kupempha, ndipo Chauta wandipatsa chopempha changacho. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Ndinapempha mwana uyu, ndipo Yehova wandipatsa chimene ndinamupempha. Onani mutuwo |