Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 1:25 - Buku Lopatulika

25 Ndipo iwo anapha ng'ombe, nabwera naye mwanayo kwa Eli.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo iwo anapha ng'ombe, nabwera naye mwanayo kwa Eli.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Kumeneko adapha ng'ombe yamphongo ija ndipo mwanayo adampereka kwa Eli.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Tsono anapha ngʼombe yamphongo ija ndi kupereka mwana uja kwa Eli.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 1:25
3 Mawu Ofanana  

Pamenepo aiphe ng'ombeyo pamaso pa Yehova; ndipo ana a Aroni, ansembewo, abwere nao mwazi, nawaze mwaziwo pozungulira paguwa la nsembe, lokhala pa khoma la chihema chokomanako.


Ndipo pamene anakwanira masiku a kukonza kwao, monga mwa chilamulo cha Mose, iwo anakwera naye kunka ku Yerusalemu, kukamsonyeza Iye kwa Ambuye,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa