1 Mbiri 4:4 - Buku Lopatulika4 ndi Penuwele atate wa Gedori, ndi Ezere atate wa Husa. Awa ndi ana a Huri woyamba wa Efurata atate wa Betelehemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 ndi Penuwele atate wa Gedori, ndi Ezere atate wa Husa. Awa ndi ana a Huri woyamba wa Efurata atate wa Betelehemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Penuwele amene adabereka Gedori ndi Ezere amene adabereka Husa. Ameneŵa anali ana a Huri, mwana wachisamba wa Efurata ndi tate wa Betelehemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Penueli anabereka Gedori, ndipo Ezeri anabereka Husa. Awa anali ana a Huri, mwana wachisamba wa Efurata ndi abambo a Betelehemu. Onani mutuwo |