Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Mbiri 4:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo Reaya mwana wa Sobala anabala Yahati; ndi Yahati anabala Ahumai, ndi Lahadi. Iwo ndiwo mabanja a Azorati.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo Reaya mwana wa Sobala anabala Yahati; ndi Yahati anabala Ahumai, ndi Lahadi. Iwo ndiwo mabanja a Azorati.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Reaya mwana wa Sobala adabereka Yahati, Yahati adabereka Ahumai ndi Lahadi. Ameneŵa ndiwo anali mabanja a Azorati.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Reaya mwana wa Sobala anabereka Yahati, ndipo Yahati anabereka Ahumai ndi Lahadi. Awa anali mabanja a Azorati.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 4:2
5 Mawu Ofanana  

Ana a Yuda: Perezi, Hezironi, ndi Karimi, ndi Huri, ndi Sobala.


Iwo ndiwo a atate wa Etamu: Yezireele, ndi Isima, ndi Idibasi; ndipo dzina la mlongo wao ndiye Hazeleleponi,


Ku chigwa, Esitaoli, ndi Zora ndi Asina;


Ndipo mzimu wa Yehova unayamba kumfulumiza mtima ku misasa ya Dani pakati pa Zora ndi Esitaoli.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa