1 Akorinto 9:13 - Buku Lopatulika13 Kodi simudziwa kuti iwo akutumikira za Kachisi amadya za mu Kachisi, ndi iwo akuimirira guwa la nsembe, agawana nalo guwa la nsembe? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Kodi simudziwa kuti iwo akutumikira za Kachisi amadya za m'Kachisi, ndi iwo akuimirira guwa la nsembe, agawana nalo guwa la nsembe? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Kodi simudziŵa kuti otumikira m'Nyumba ya Mulungu, amadya chakudya cha m'Nyumbamo, ndipo kuti opereka nsembe pa guwa lansembe, amalandira nao zansembezo? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Kodi simukudziwa kuti wogwira ntchito mʼNyumba ya Mulungu amapeza chakudya chawo mʼNyumbamo, ndipo kuti otumikira pa guwa lansembe amagawana zimene zaperekedwa pa guwa lansembelo. Onani mutuwo |