1 Akorinto 8:9 - Buku Lopatulika9 Koma yang'anirani kuti ulamuliro wanu umene ungakhale chokhumudwitsa ofookawo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Koma yang'anirani kuti ulamuliro wanu umene ungakhale chokhumudwitsa ofookawo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Komabe chenjerani kuti ufulu wanuwu pochita zinthu, ungaphunthwitse ena amene chikhulupiriro chao nchosalimba kwenikweni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Komabe samalani kuti ufulu wanu ochita zinthu usafike pokhumudwitsa ofowoka. Onani mutuwo |