1 Akorinto 8:8 - Buku Lopatulika8 Koma chakudya sichitivomerezetsa kwa Mulungu; kapena ngati sitidya sitisowa; kapena ngati tidya tilibe kupindulako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Koma chakudya sichitivomerezetsa kwa Mulungu; kapena ngati sitidya sitisowa; kapena ngati tidya tilibe kupindulako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Nzoona kuti chakudya sichitifikitsa pafupi ndi Mulungu. Tikapanda kudya chakudyacho, sititayapo kanthu, komanso tikachidya, sitipindulapo kanthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Koma chakudya sichitisendeza kufupi ndi Mulungu. Tikapanda kudya si vuto, tikadya sitisinthikanso. Onani mutuwo |