1 Akorinto 8:10 - Buku Lopatulika10 Pakuti wina akaona iwe amene uli nacho chidziwitso, ulikukhala pachakudya mu Kachisi wa fano, kodi chikumbumtima chake, popeza ali wofooka, sichidzalimbika kudya zoperekedwa nsembe kwa mafano? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Pakuti wina akaona iwe amene uli nacho chidziwitso, ulikukhala pachakudya m'Kachisi wa fano, kodi chikumbu mtima chake, popeza ali wofooka, sichidzalimbika kudya zoperekedwa nsembe kwa mafano? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ngati iweyo amene uli wodziŵa udya m'nyumba yopembedzeramo fano, nanga tsono munthu wosadziŵa kwenikweni, atakuwona ukuchita zimenezi, kodi chimenechi sichidzamlimbitsa mtima kuti nayenso azidya chakudya choperekedwa kwa mafano? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Pakuti ngati aliyense wachikumbumtima chofowoka akakuonani achidziwitsonu mukudya mʼnyumba yopembedzera mafano, kodi iyeyo sichidzamulimbitsa mtima kuti azidya chakudya choperekedwa nsembe kwa mafano? Onani mutuwo |