1 Akorinto 8:2 - Buku Lopatulika2 Ngati wina ayesa kuti adziwa kanthu sanayambe kudziwa monga ayenera kudziwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ngati wina ayesa kuti adziwa kanthu sanayambe kudziwa monga ayenera kudziwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Munthu amene amadziyesa wodziŵa kanthu, ndiye kuti sakudziŵabe kwenikweni monga momwe akadayenera kudziŵira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Munthu amene amaganiza kuti amadziwa kanthu, ndiye kuti sakudziwa monga mmene amayenera kudziwira. Onani mutuwo |