1 Akorinto 8:1 - Buku Lopatulika1 Koma za zoperekedwa nsembe kwa mafano: Tidziwa kuti tili nacho chidziwitso tonse. Chidziwitso chitukumula, koma chikondi chimangirira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Koma za zoperekedwa nsembe kwa mafano: Tidziwa kuti tili nacho chidziwitso tonse. Chidziwitso chitukumula, koma chikondi chimangirira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsopano ndifuna kunena za chakudya choperekedwa kwa mafano. Nzoonadi kuti tonse tili nazo nzeru, komatu nzeru zokha zimangotukumula anthu. Chikondi ndicho chimapindulitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tsopano za chakudya choperekedwa nsembe kwa mafano: Ife tidziwa kuti tonse tili ndi chidziwitso. Komatu chidziwitso chokha chimadzitukumula, koma chikondi ndicho chimapindulitsa. Onani mutuwo |