1 Akorinto 8:3 - Buku Lopatulika3 Koma ngati wina akonda Mulungu, yemweyu adziwika ndi Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Koma ngati wina akonda Mulungu, yemweyu adziwika ndi Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Koma munthu akamakonda Mulungu, ndiye kuti amadziŵika ndi Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Koma munthu amene amakonda Mulungu amadziwika ndi Mulunguyo. Onani mutuwo |