1 Akorinto 7:9 - Buku Lopatulika9 Koma ngati sadziwa kudziletsa, akwatitsidwe; pakuti nkwabwino kukwatira koposa kutentha mtima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Koma ngati sadziwa kudziletsa, akwatitsidwe; pakuti nkwabwino kukwatira koposa kutentha mtima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Koma ngati sangathe kudziletsa, aloŵe m'banja, pakuti nkwabwino kuloŵa m'banja kupambana kupsa ndi moto wa zilakolako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Koma ngati sangathe kudziretsa, akwatire, popeza ndi bwino kukwatira kusiyana ndi kudzizunza ndi chilakolako. Onani mutuwo |