Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Akorinto 7:27 - Buku Lopatulika

27 Kodi wamangika kwa mkazi? Usafune kumasuka. Kodi wamasuka kwa mkazi? Usafune mkazi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Kodi wamangika kwa mkazi? Usafune kumasuka. Kodi wamasuka kwa mkazi? Usafune mkazi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Kodi ndiwe wapabanja? Usayese kuthetsa banja lako. Kodi ndiwe wopanda banja? Usayese kupeza banja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Kodi ndinu wokwatira? Musalekane. Kodi ndinu wosakwatira? Musafunefune mkazi.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 7:27
4 Mawu Ofanana  

Yense akhale m'maitanidwe m'mene anaitanidwamo.


Chifukwa chake ndiyesa kuti ichi ndi chokoma chifukwa cha chivuto cha nyengo ino, kuti nkwabwino kwa munthu kukhala monga ali.


Koma ungakhale ukwatira, sunachimwe; ndipo ngati namwali akwatiwa, sanachimwe. Koma otere adzakhala nacho chisautso m'thupi, ndipo ndikulekani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa