Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Akorinto 7:20 - Buku Lopatulika

20 Yense akhale m'maitanidwe m'mene anaitanidwamo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Yense akhale m'maitanidwe m'mene anaitanidwamo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Aliyense angokhala monga momwe analiri pamene Mulungu adamuitana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Aliyense akhale monga analili pamene Mulungu anamuyitana.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 7:20
7 Mawu Ofanana  

Monga mbalame yosochera kuchisa chake, momwemo munthu wosochera kumalo ake.


Koma, monga Ambuye wagawira kwa yense, monga Mulungu waitana yense, momwemo ayende. Ndipo kotero ndiika mu Mipingo yonse.


Kodi wamangika kwa mkazi? Usafune kumasuka. Kodi wamasuka kwa mkazi? Usafune mkazi.


ndi kuti muyesetse kukhala chete ndi kuchita za inu eni ndi kugwira ntchito ndi manja anu, monga tinakuuzani;


Koma oterewa tiwalamulira ndi kuwadandaulira mwa Ambuye Yesu Khristu, kuti agwire ntchito pokhala chete, nadye chakudya cha iwo okha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa