1 Akorinto 7:1 - Buku Lopatulika1 Koma za izi munalembazi; kuli bwino kwa munthu kusakhudza mkazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Koma za izi munalembazi; kuli bwino kwa munthu kusakhudza mkazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsopano ndiyankhe zimene mudandifunsa m'kalata yanu. Nkwabwino kuti munthu asakwatire, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tsopano pa zinthu zomwe munandilembera nʼkwabwino kuti munthu asakwatire. Onani mutuwo |