1 Akorinto 5:4 - Buku Lopatulika4 m'dzina la Ambuye wathu Yesu, posonkhana pamodzi inu ndi mzimu wanga, ndi mphamvu ya Ambuye wathu Yesu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 m'dzina la Ambuye wathu Yesu, posonkhana pamodzi inu ndi mzimu wanga, ndi mphamvu ya Ambuye wathu Yesu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Tsono mutasonkhana m'dzina la Ambuye Yesu, inenso m'maganizo ndili nanu pomwepo, ndi mphamvu ya Ambuye athu Yesu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mukasonkhana mu dzina la Ambuye athu Yesu, ine ndili nanu mu mzimu, ndipo mphamvu ya Ambuye athu Yesu ili pomwepo, Onani mutuwo |