1 Akorinto 5:13 - Buku Lopatulika13 koma akunja awaweruza Mulungu? Chotsani woipayo pakati pa inu nokha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 koma akunja awaweruza Mulungu? Chotsani woipayo pakati pa inu nokha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ndi Mulungu amene amaweruza anthu akunjawo. Paja mau a Mulungu akuti, “Munthu woipayo mumchotse pakati panu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Mulungu adzaweruza akunja. “Chotsani woyipayo pakati panu.” Onani mutuwo |
Ndipo mneneriyo, kapena wolota malotoyo, mumuphe; popeza ananena chosiyanitsa ndi Yehova Mulungu wanu, amene anakutulutsani m'dziko la Ejipito, nakuombolani m'nyumba ya ukapolo; kuti akucheteni mutaye njira imene Yehova Mulungu wanu anakulamulirani muziyendamo. Potero muzichotsa choipacho pakati pa inu.