1 Akorinto 4:12 - Buku Lopatulika12 ndipo tigwiritsa ntchito, ndi kuchita ndi manja athu a ife tokha; polalatidwa tidalitsa; pozunzidwa, tipirira; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 ndipo tigwiritsa ntchito, ndi kuchita ndi manja athu a ife tokha; polalatidwa tidalitsa; pozunzidwa, tipirira; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Tikugwira ntchito kolimba ndi manja athu kuti tidzisunge. Anthu akamatichita chipongwe, timapempha kuti Mulungu aŵadalitse. Anthu akamatizunza, timangopirira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Timagwira ntchito molimbika ndi manja athu. Akamatitemberera, ife timadalitsa; tikasautsidwa, ife timapirira. Onani mutuwo |