1 Akorinto 3:7 - Buku Lopatulika7 Chotero sali kanthu kapena wookayo, kapena wothirirayo; koma Mulungu amene akulitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Chotero sali kanthu kapena wookayo, kapena wothirirayo; koma Mulungu amene akulitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Motero wobzala kapenanso wothirira sali kanthu, koma Mulungu yekha amene amameretsa, ndiye ali kanthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Choncho kuphatikiza iye wodzala ndi iye wothirira, onse sali kanthu, koma Mulungu yekha amene amakulitsa zinthu. Onani mutuwo |