1 Akorinto 3:6 - Buku Lopatulika6 Ndinaoka ine, anathirira Apolo; koma Mulungu anakulitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndinaoka ine, anathirira Apolo; koma Mulungu anakulitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ineyo ndidabzala mbeu, Apolo nkuzithirira, koma amene adazimeretsa ndi Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ine ndinadzala mbewu, Apolo anayithirira, koma Mulungu ndiye anayikulitsa. Onani mutuwo |