1 Akorinto 2:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo ine ndinakhala nanu mofooka ndi m'mantha, ndi monthunthumira mwambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo ine ndinakhala nanu mofooka ndi m'mantha, ndi monthunthumira mwambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Choncho pamene ndidafika kwanuko, ndinali wofooka, ndiponso ndinkanjenjemera kwambiri ndi mantha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ndinabwera kwa inu wofowoka ndi wamantha, ndiponso wonjenjemera kwambiri. Onani mutuwo |