1 Akorinto 2:15 - Buku Lopatulika15 Koma iye amene ali wauzimu ayesa zonse, koma iye yekha sayesedwa ndi mmodzi yense. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Koma iye amene ali wauzimu ayesa zonse, koma iye yekha sayesedwa ndi mmodzi yense. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Munthu amene ali ndi Mzimu Woyera angathe kuzindikira khalidwe la zonse, ndipo palibe wina amene angathe kutsutsapo ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Munthu wauzimu amaweruza pa zinthu zonse, koma iye mwini saweruzidwa ndi munthu aliyense. Onani mutuwo |