1 Akorinto 16:6 - Buku Lopatulika6 ndipo kapena ndidzakhalitsa ndi inu, kapenanso kugonera nyengo yachisanu kuti mukandiperekeze ine kumene kulikonse ndipitako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 ndipo kapena ndidzakhalitsa ndi inu, kapenanso kugonera nyengo yachisanu kuti mukandiperekeze ine kumene kulikonse ndipitako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Koma kapena kwanuko ndidzakhala kanthaŵi, kapenanso nyengo yonse yachisanu. Ndifuna kuti pambuyo pake mudzandithandize kupitiriza ulendo wanga kulikonse kumene ndingapite. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Mwina ndidzakhala nanu kanthawi kochepa kapenanso nyengo yonse yozizira, kuti mudzandithandize kupitiriza ulendo wanga kulikonse kumene ndingapite. Onani mutuwo |