1 Akorinto 16:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo ngati kuyenera kwa ine kupitanso, adzapita nane. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo ngati kuyenera kwa ine kupitanso, adzapita nane. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Koma ngati nkofunika kuti inenso ndipite, tidzapitira limodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ngati kutaoneka kuti nʼkoyenera kuti ndipite nawo, adzapita nane limodzi. Onani mutuwo |