Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Akorinto 16:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo ngati kuyenera kwa ine kupitanso, adzapita nane.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo ngati kuyenera kwa ine kupitanso, adzapita nane.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Koma ngati nkofunika kuti inenso ndipite, tidzapitira limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Ngati kutaoneka kuti nʼkoyenera kuti ndipite nawo, adzapita nane limodzi.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 16:4
5 Mawu Ofanana  

Koma tsopano ndipita ku Yerusalemu, ndilikutumikira oyera mtima.


Ndipo pamene ndifika, ndidzatuma iwo amene mudzawayesa oyenera, ndi makalata, apite nayo mphatso yanu ku Yerusalemu.


Koma ndidzadza kwa inu, nditapyola Masedoniya; pakuti ndidzapyola Masedoniya;


ndipo si ichi chokha, komanso anasankhika ndi Mipingo, apite limodzi ndi ife m'chisomo ichi, chimene tichitumikira ife, kwa ulemerero wa Ambuye, ndi kuonetsa chivomerezo chathu;


anachita eni ake, natiumiriza ndi kutidandaulira za chisomocho, ndi za chiyanjano cha utumiki wa kwa oyera mtima;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa