1 Akorinto 16:16 - Buku Lopatulika16 kuti inunso muvomere otere, ndi yense wakuchita nao, ndi kugwiritsa ntchito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 kuti inunso muvomere otere, ndi yense wakuchita nao, ndi kugwiritsa ntchito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Tsono ndikukupemphani kuti inunso muziŵamvera anthu otere, ndiponso aliyense wogwira ntchito ndi kutumikira modzipereka pamodzi nawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 kuti muziwamvera anthu oterewa, ndiponso aliyense wogwira nawo ntchitoyi modzipereka. Onani mutuwo |