1 Akorinto 16:17 - Buku Lopatulika17 Koma ndikondwera pa kudza kwao kwa Stefanasi, ndi Fortunato, ndi Akaiko; chifukwa iwo anandikwaniritsa chotsalira chanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Koma ndikondwera pa kudza kwao kwa Stefanasi, ndi Fortunato, ndi Akaiko; chifukwa iwo anandikwaniritsa chotsalira chanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Ndakondwa kuti Stefanasi, Fortunato ndi Akaiko afika, pakuti ngakhale inu simuli nane, iwo achita ngati kuloŵa m'malo wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Ndikondwera kuti Stefano, Fortunato ndi Akayiko afika, chifukwa akhala akundithandiza pakuti inu simuli nane. Onani mutuwo |