1 Akorinto 15:5 - Buku Lopatulika5 ndi kuti anaonekera kwa Kefa; pamenepo kwa khumi ndi awiriwo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 ndi kuti anaonekera kwa Kefa; pamenepo kwa khumi ndi awiriwo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Motero adaonekera Kefa, kenaka atumwi khumi ndi aŵiri aja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 ndipo kuti anaonekera kwa Petro, ndipo kenaka kwa Atumwi khumi ndi awiriwo. Onani mutuwo |