1 Akorinto 15:4 - Buku Lopatulika4 ndi kuti anaikidwa; ndi kuti anaukitsidwa tsiku lachitatu, monga mwa malembo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 ndi kuti anaikidwa; ndi kuti anaukitsidwa tsiku lachitatu, monga mwa malembo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Adaikidwa m'manda, mkucha wake adauka, monga Malembo anenera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 kuti anayikidwa mʼmanda, kuti anaukitsidwa tsiku lachitatu monga mwa Malemba; Onani mutuwo |