1 Akorinto 15:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti ndinapereka kwa inu poyamba, chimenenso ndinalandira, kuti Khristu anafera zoipa zathu, monga mwa malembo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti ndinapereka kwa inu poyamba, chimenenso ndinalandira, kuti Khristu anafera zoipa zathu, monga mwa malembo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pajatu mau aakulu amene ndidakupatsani ndi omwewo amene inenso ndidalandira. Mauwo ndi akuti Khristu adafera machimo athu, monga Malembo anenera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pakuti chimene ndinalandira ndinapereka kwa inu monga chofunika kuposa zonse, kuti Khristu anafera zoyipa zathu monga mwa Malemba, Onani mutuwo |