1 Akorinto 15:2 - Buku Lopatulika2 umenenso mupulumutsidwa nao ngati muugwiritsa monga momwe ndinalalikira kwa inu; ngati simunakhulupirire chabe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 umenenso mupulumutsidwa nao ngati muugwiritsa monga momwe ndinalalikira kwa inu; ngati simunakhulupirira chabe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mulungu adzakupulumutsani ndi Uthenga Wabwinowu, ngati musunga bwino mau ake monga ndidakulalikirani. Popanda kutero, bwenzi mutangokhulupirira pachabe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Inu munapulumutsidwa ndi Uthenga Wabwinowu, ngati mwasunga mawu amene ndinakulalikirani. Kupanda kutero, mwangokhulupirira pachabe. Onani mutuwo |