1 Akorinto 15:6 - Buku Lopatulika6 pomwepo anaoneka pa nthawi imodzi kwa abale oposa mazana asanu, amene ochuluka a iwo akhala kufikira tsopano, koma ena agona; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 pomwepo anaoneka pa nthawi imodzi kwa abale oposa mazana asanu, amene ochuluka a iwo akhala kufikira tsopano, koma ena agona; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pambuyo pake adaonekera abale opitirira mazana asanu pa nthaŵi imodzi. Ambiri mwa iwowo akalipo, ena adamwalira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pambuyo pake, Iye anaonekera kwa anthu oposa 500 mwa abale pa nthawi imodzi, ndipo ambiri mwa iwo akanali ndi moyo ngakhale kuti ena anagona tulo. Onani mutuwo |