Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Akorinto 15:12 - Buku Lopatulika

12 Koma ngati Khristu alalikidwa kuti waukitsidwa kwa akufa, nanga ena mwa inu anena bwanji kuti kulibe kuuka kwa akufa?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Koma ngati Khristu alalikidwa kuti waukitsidwa kwa akufa, nanga ena mwa inu anena bwanji kuti kulibe kuuka kwa akufa?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Tsono popeza kuti chimene timalalika ndi chakuti Khristu adauka kwa akufa, bwanji ena mwa inu akunena kuti, “Anthu akufa sadzaukanso?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Koma ngati timalalikira kuti Khristu anaukitsidwa kwa akufa, zikutheka bwanji kuti ena mwa inu azinena kuti kulibe kuuka kwa akufa?

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 15:12
7 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene anamva za kuuka kwa akufa ena anaseka pwepwete; koma ena anati, Tidzakumvanso za chimenechi.


Pakutitu Asaduki anena kuti kulibe kuuka kwa akufa, kapena mngelo, kapena mzimu; koma Afarisi avomereza ponse pawiri.


Muchiyesa chinthu chosakhulupirika, chakuti Mulungu aukitsa akufa?


Ngati ine tsono, kapena iwowa, kotero tilalikira, ndi kotero munakhulupirira.


asangalatse mitima yanu, nakhazikitse inu mu ntchito yonse ndi mau onse abwino.


ndiwo amene adasokera kunena za choonadi, ponena kuti kuuka kwa akufa kwachitika kale, napasula chikhulupiriro cha ena.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa