1 Akorinto 14:4 - Buku Lopatulika4 Iye wakulankhula lilime, adzimangirira yekha, koma iye wakunenera amangirira Mpingo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Iye wakulankhula lilime, adzimangirira yekha, koma iye wakunenera amangirira Mpingo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Munthu wolankhula chilankhulo chosadziŵika, amangothandizidwa yekha, koma wolankhula mau ochokera kwa Mulungu, amathandiza mpingo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Iye amene amayankhula malilime amadzilimbikitsa yekha, koma amene amanenera amalimbikitsa mpingo. Onani mutuwo |