1 Akorinto 14:3 - Buku Lopatulika3 Koma iye wakunenera alankhula ndi anthu chomangirira ndi cholimbikitsa, ndi chosangalatsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Koma iye wakunenera alankhula ndi anthu chomangirira ndi cholimbikitsa, ndi chosangalatsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Koma wolankhula mau ochokera kwa Mulungu, amalankhula ndi anthu, ndipo amaŵathandiza, amaŵalimbitsa mtima ndi kuŵasangalatsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Koma amene amanenera amayankhula kwa anthu kuti awapatse mphamvu, awalimbikitse ndi kuwakhazikitsa mtima pansi. Onani mutuwo |