1 Akorinto 13:5 - Buku Lopatulika5 sichichita zosayenera, sichitsata za mwini yekha, sichipsa mtima, sichilingirira zoipa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 sichichita zosayenera, sichitsata za mwini yekha, sichipsa mtima, sichilingirira zoipa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Chikondi chilibe matama kapena chipongwe, sichidzikonda, sichikwiya, sichisunga mangaŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Chikondi chilibe mwano, sichodzikonda, sichipsa mtima msanga, sichisunga mangawa. Onani mutuwo |