1 Akorinto 13:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo tsopano zitsala zitatu izi: chikhulupiriro, chiyembekezo, chikondi; koma chachikulu cha izi ndicho chikondi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo tsopano zitsala chikhulupiriro, chiyembekezo, chikondi, zitatu izi; koma chachikulu cha izi ndicho chikondi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Choncho pakali pano zilipo zinthu zitatuzi: chikhulupiriro, chiyembekezo ndi chikondi. Koma mwa zonsezi chopambana ndi chikondi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndipo tsopano zatsala zinthu zitatu: chikhulupiriro, chiyembekezo ndi chikondi. Koma chachikulu pa zonsezi ndi chikondi. Onani mutuwo |