1 Akorinto 14:1 - Buku Lopatulika1 Tsatani chikondi; koma funitsitsani mphatso zauzimu, koma koposa kuti mukanenere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Tsatani chikondi; koma funitsitsani mphatso zauzimu, koma koposa kuti mukanenere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Muziyesetsa kukhala nacho chikondi, komanso muike mtima pa mphatso zimene Mzimu Woyera amapereka, makamaka mphatso ya kulankhula mau ochokera kwa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Funafunani chikondi, ndikufunitsitsa mphatso zauzimu, makamaka mphatso ya uneneri. Onani mutuwo |