1 Akorinto 12:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo pali machitidwe osiyana, koma Mulungu yemweyo, wakuchita zinthu zonse mwa onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo pali machitidwe osiyana, koma Mulungu yemweyo, wakuchita zinthu zonse mwa onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pali mphamvu zosiyanasiyana, koma Mulungu ndi mmodzimodzi amene amagwiritsa ntchito mphamvu zonsezo mwa munthu aliyense. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pali magwiridwe antchito osiyanasiyana, koma Mulungu yemweyo amagwira ntchito monsemo mwa anthu onse. Onani mutuwo |