1 Akorinto 12:7 - Buku Lopatulika7 Koma kwa yense kwapatsidwa maonekedwe a Mzimu kuti apindule nao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Koma kwa yense kwapatsidwa maonekedwe a Mzimu kuti apindule nao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Mzimu Woyera amapatsa munthu aliyense mphatso yakutiyakuti yoti aigwiritse ntchito yopindulitsa anthu onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Tsono Mzimu amapereka mphatso kwa aliyense kuti ipindulire onse. Onani mutuwo |