1 Akorinto 12:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo ngati khutu likati, Popeza sindili diso, sindili wa thupi; kodi silili la thupi chifukwa cha ichi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo ngati khutu likati, Popeza sindili diso, sindili wa thupi; kodi silili la thupi chifukwa cha ichi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Nanga khutu litanena kuti, “Poti sindine diso, ndiye kuti sindine chiwalo cha thupi”, kodi silikhala chiwalo cha thupi chifukwa cha chimenecho? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ndipo ngati khutu litanena kuti, “Pakuti sindine diso, sindine chiwalo cha thupi.” Chifukwa chimenechi sichingachititse khutu kuti lisakhale chiwalo cha thupi. Onani mutuwo |