1 Akorinto 12:17 - Buku Lopatulika17 Ngati thupi lonse likadakhala diso, kukadakhala kuti kununkhiza? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ngati thupi lonse likadakhala diso, kukadakhala kuti kununkhiza? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Kodi thupi lonse likadakhala diso lokha, bwenzi munthu akumva bwanji? Kapena thupi lonse likadakhala khutu lokha, bwenzi munthu akununkhiza bwanji? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Kodi thupi lonse likanakhala diso, tikanamamva bwanji? Nanga thupi lonse likanakhala khutu, tikanamanunkhiza bwanji? Onani mutuwo |