1 Akorinto 11:9 - Buku Lopatulika9 pakutinso mwamuna sanalengedwe chifukwa cha mkazi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 pakutinso mwamuna sanalengedwa chifukwa cha mkazi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ndiponso mwamuna sadalengedwe chifukwa cha mkazi, koma mkazi ndiye adalengedwa chifukwa cha mwamuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndipo mwamuna sanalengedwe chifukwa cha mkazi, koma mkazi analengedwera mwamuna. Onani mutuwo |