Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Akorinto 11:21 - Buku Lopatulika

21 pakuti pakudyaku yense ayamba watenga mgonero wake wa yekha, ndipo wina ali ndi njala, ndi wina aledzera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 pakuti pakudyaku yense athanga watenga mgonero wake wa yekha, ndipo wina ali ndi njala, ndi wina aledzera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Inu mumati mukamadya, aliyense angoyambapo kudya chakudya chakechake, kotero kuti wina amakhala ndi njala, m'menemo wina waledzera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Pakuti mukamadya, aliyense amangodzidyera zomwe anakonza. Wina amakhala ndi njala pamene wina amaledzera.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 11:21
7 Mawu Ofanana  

nanena naye, Munthu aliyense amayamba kuika vinyo wokoma; ndipo anthu atamwatu, pamenepo wina wosakoma; koma iwe wasunga vinyo wokoma kufikira tsopano lino.


Chifukwa chake, pakusonkhana inu pamodzi sikutheka kudya mgonero wa Ambuye;


Ngati wina ali ndi njala adye kwao; kuti mungasonkhanire kwa chiweruziro. Koma zotsalazo ndidzafotokoza pakudza ine.


ochitidwa zoipa kulipira kwa chosalungama; anthu akuyesera chowakondweretsa kudyerera usana; ndiwo mawanga ndi zilema, akudyerera m'madyerero achikondi ao, pamene akudya nanu;


Iwo ndiwo okhala mawanga pa maphwando anu a chikondano, pakudya nanu pamodzi, akudziweta okha opanda mantha; mitambo yopanda madzi, yotengekatengeka ndi mphepo; mitengo ya masika yopanda zipatso, yofafa kawiri, yozuka mizu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa