1 Akorinto 11:11 - Buku Lopatulika11 Komanso mkazi sakhala wopanda mwamuna, kapena mwamuna wopanda mkazi, mwa Ambuye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Komanso mkazi sakhala wopanda mwamuna, kapena mwamuna wopanda mkazi, mwa Ambuye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Komabe m'maso mwa Ambuye mkazi sali kanthu popanda mwamuna, ndiponso mwamuna sali kanthu popanda mkazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Komabe mwa Ambuye, mkazi amadalira mwamuna ndipo mwamuna amadalira mkazi. Onani mutuwo |