1 Akorinto 10:30 - Buku Lopatulika30 Ngati ine ndilandirako mwachisomo, ndinenezedwa bwanji chifukwa cha ichi chimene ndiyamikapo? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ngati ine ndilandirako mwachisomo, ndinenezedwa bwanji chifukwa cha ichi chimene ndiyamikapo? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Ngati ine ndikuthokoza Mulungu chifukwa cha chakudya changa, nanga munthu angandinyoze bwanji chifukwa cha chakudya chimene ndikuchilandira mothokoza Mulungu?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Ngati ndikuyamika Mulungu chifukwa cha chakudya, nanga munthu angandinyoze bwanji pa zinthu zomwe ndayamikira nazo Mulungu? Onani mutuwo |