1 Akorinto 10:31 - Buku Lopatulika31 Chifukwa chake mungakhale mudya, mungakhale mumwa, mungakhale muchita kanthu kena, chitani zonse ku ulemerero wa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Chifukwa chake mungakhale mudya, mungakhale mumwa, mungakhale muchita kanthu kena, chitani zonse ku ulemerero wa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Tsono, kaya mulikudya, kaya mulikumwa, kaya mukuchita chilichonse, muzichita zonse kuti mulemekeze Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Nʼchifukwa chake chilichonse mungadye kapena kumwa, kapena chimene mungachite, chitani zonse ku ulemerero wa Mulungu. Onani mutuwo |