1 Akorinto 10:26 - Buku Lopatulika26 pakuti dziko lapansi lili la Ambuye, ndi kudzala kwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 pakuti dziko lapansi lili la Ambuye, ndi kudzala kwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Paja Malembo akuti, “Dziko lapansi ndi zonse zam'menemo ndi za Chauta.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Popeza kuti, “Dziko lapansi ndi la Ambuye ndi zonse za mʼmenemo ndi zake.” Onani mutuwo |