1 Akorinto 10:25 - Buku Lopatulika25 Chonse chogulitsidwa pa msika wa nyama, mudye, osafunsa kanthu chifukwa cha chikumbumtima; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Chonse chogulitsidwa pa msika wa nyama, mudye, osafunsa kanthu chifukwa cha chikumbu mtima; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Mungathe kudya nyama iliyonse imene amagulitsa pa msika, osafunsa mafunso okhudzana ndi m'mene mtima wanu umamvera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Idyani nyama iliyonse imene amagulitsa pa msika, osafunsa mafunso okhudzana ndi chikumbumtima chanu. Onani mutuwo |