1 Akorinto 10:18 - Buku Lopatulika18 Tapenyani Israele monga mwa thupi; kodi iwo akudya nsembezo alibe chiyanjano ndi guwa la nsembe? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Tapenyani Israele monga mwa thupi; kodi iwo akudya nsembezo alibe chiyanjano ndi guwa la nsembe? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Onani zimene amachita Ayuda. Nanga amene amadyako zoperekedwa nsembe, kodi suja amachita nao miyambo ya pa guwa lansembelo? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Taganizirani zimene amachita Aisraeli. Kodi onse amene amadya zoperekedwa nsembe, samachita nawo miyambo ya pa guwapo? Onani mutuwo |